Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 40:11, 12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiye Ayuda onse amene anali ku Mowabu, ku Amoni, ku Edomu komanso amene anali mʼmayiko ena onse anamvanso kuti mfumu ya Babulo yalola kuti anthu amene anatsala azikhala ku Yuda komanso kuti yaika Gedaliya mwana wa Ahikamu mwana wa Safani kuti aziwalamulira. 12 Choncho Ayuda onse anayamba kubwerera kuchokera kumadera onse kumene anawabalalitsira ndipo anabwera mʼdziko la Yuda kwa Gedaliya ku Mizipa. Iwo anasonkhanitsa vinyo ndi zipatso zamʼchilimwe zochuluka kwambiri.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani