Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 6:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Atatero ndinafunsa kuti: “Mpaka liti, inu Yehova?” Iye anayankha kuti:

      “Mpaka mizinda yawo itawonongedwa nʼkukhala mabwinja

      Mpaka nyumba zawo zitakhala zopanda anthu okhalamo

      Ndiponso mpaka dziko litawonongekeratu nʼkukhala bwinja.+

  • Yeremiya 39:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Kenako Akasidi anawotcha nyumba ya mfumu ndi nyumba za anthu+ ndipo anagwetsa mpanda wa Yerusalemu.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani