-
Yesaya 6:11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 Atatero ndinafunsa kuti: “Mpaka liti, inu Yehova?” Iye anayankha kuti:
“Mpaka mizinda yawo itawonongedwa nʼkukhala mabwinja
Mpaka nyumba zawo zitakhala zopanda anthu okhalamo
Ndiponso mpaka dziko litawonongekeratu nʼkukhala bwinja.+
-