Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 15:4-6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Hesiboni ndi Eleyale+ akulira mofuula.

      Mawu awo akumveka mpaka ku Yahazi.+

      Nʼchifukwa chake amuna onyamula zida a ku Mowabu akungofuula.

      Iwo akunjenjemera kwambiri.

       5 Mtima wanga ukulirira Mowabu.

      Anthu ake athawira kutali, ku Zowari+ ndi ku Egilati-selisiya.+

      Iwo akulira pamene akukwera mtunda wa Luhiti.

      Panjira yopita ku Horonaimu, iwo akulira kwambiri chifukwa cha tsokalo.+

       6 Madzi a ku Nimurimu aumiratu.

      Msipu wobiriwira wauma,

      Udzu watha ndipo palibenso chilichonse chobiriwira chimene chatsala.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani