Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Numeri 24:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ndidzamuona, koma osati panopa;

      Ndidzamupenya, koma osati posachedwa.

      Nyenyezi+ idzatuluka mwa Yakobo,

      Ndodo yachifumu+ idzatuluka mu Isiraeli.+

      Ndipo iye adzaphwanyadi chipumi cha Mowabu+

      Ndi mitu ya asilikali onse ankhanza.

  • Amosi 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Choncho ndidzatumiza moto ku Mowabu,

      Ndipo udzawotcheratu nsanja zolimba za Kerioti.+

      Mowabu adzafa pakati pa phokoso,

      Pakati pa mfuu yankhondo ndiponso kulira kwa lipenga la nyanga ya nkhosa.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani