Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Obadiya 2-4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 “Taona! Ndakuchititsa kukhala wosafunika pakati pa mitundu ina,

      Ndipo ikukuona kuti ndiwe wonyozeka kwambiri.+

       3 Mtima wako wodzikuza wakupusitsa,+

      Iwe amene ukukhala mʼmalo obisika amʼthanthwe,

      Uli pamwamba pa phiri nʼkumanena mumtima mwako kuti,

      ‘Ndani angandigwetsere pansi?’

       4 Ngakhale utamakhala mʼmwamba* ngati chiwombankhanga,

      Kapena utamanga chisa chako pakati pa nyenyezi,

      Ine ndidzakugwetsapo pamenepo,” akutero Yehova.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani