Deuteronomo 31:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Pa nthawi imeneyo mkwiyo wanga udzawayakira+ ndipo ndidzawasiya+ nʼkuwabisira nkhope yanga+ mpaka atawonongedwa.+ Ndiyeno akadzakumana ndi masoka komanso mavuto ambiri adzanena kuti, ‘Masoka amenewatu akutigwera chifukwa chakuti Mulungu wathu sali pakati pathu.’+ Yesaya 27:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Tinthambi take tikadzauma,Akazi adzabwera kudzatithyolaNʼkukakolezera moto. Anthu awa samvetsa zinthu,+ Nʼchifukwa chake amene anawapanga sadzawachitira chifundo,Ndipo amene anawaumba sadzawakomera mtima.+ Yesaya 63:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Koma iwo anapanduka+ nʼkumvetsa chisoni mzimu wake woyera.+ Kenako iye anakhala mdani wawo,+Ndipo anachita nawo nkhondo.+
17 Pa nthawi imeneyo mkwiyo wanga udzawayakira+ ndipo ndidzawasiya+ nʼkuwabisira nkhope yanga+ mpaka atawonongedwa.+ Ndiyeno akadzakumana ndi masoka komanso mavuto ambiri adzanena kuti, ‘Masoka amenewatu akutigwera chifukwa chakuti Mulungu wathu sali pakati pathu.’+
11 Tinthambi take tikadzauma,Akazi adzabwera kudzatithyolaNʼkukakolezera moto. Anthu awa samvetsa zinthu,+ Nʼchifukwa chake amene anawapanga sadzawachitira chifundo,Ndipo amene anawaumba sadzawakomera mtima.+
10 Koma iwo anapanduka+ nʼkumvetsa chisoni mzimu wake woyera.+ Kenako iye anakhala mdani wawo,+Ndipo anachita nawo nkhondo.+