Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 29:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 ‘Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti: “Ine ndikuwatumizira lupanga, njala ndi mliri*+ ndipo ndidzawachititsa kuti akhale ngati nkhuyu zowola* zimene ndi zoipa kwambiri moti munthu sangadye.”’+

  • Yeremiya 38:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Yehova wanena kuti, ‘Amene atsale mumzinda uno adzafa ndi lupanga, njala ndi mliri.*+ Koma amene adzadzipereke* kwa Akasidi adzapitiriza kukhala ndi moyo. Adzapulumutsa moyo wake, sadzafa ayi.’+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani