Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Salimo 107:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Chifukwa anapandukira mawu a Mulungu,

      Ananyoza malangizo a Wamʼmwambamwamba.+

  • Yesaya 1:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Imvani inu okhala kumwamba, ndipo tcherani khutu inu okhala padziko lapansi,+

      Chifukwa Yehova wanena kuti:

      “Ndalera ana nʼkuwasamalira kuti akule,+

      Koma iwo andipandukira.+

  • Yesaya 63:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma iwo anapanduka+ nʼkumvetsa chisoni mzimu wake woyera.+

      Kenako iye anakhala mdani wawo,+

      Ndipo anachita nawo nkhondo.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani