Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Deuteronomo 32:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Kunja, lupanga lidzawasandutsa anamfedwa.+

      Mʼnyumba, anthu adzagwidwa ndi mantha+

      Zimenezi zidzachitikira mnyamata, namwali,

      Mwana wamngʼono ndi munthu wa imvi.+

  • Yeremiya 15:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndiyeno akakufunsa kuti, ‘Tipite kuti?’ uwayankhe kuti, ‘Yehova wanena kuti:

      “Amene akuyenera kufa ndi mliri afe ndi mliri!

      Amene akuyenera kufa ndi lupanga afe ndi lupanga!+

      Amene akuyenera kufa ndi njala yaikulu afe ndi njala yaikulu!

      Amene akuyenera kutengedwa kupita ku ukapolo atengedwe kupita ku ukapolo!”’+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani