Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mafumu 17:7, 8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Zimenezi zinachitika chifukwa chakuti Aisiraeli anachimwira Yehova Mulungu wawo, yemwe anawatulutsa mʼdziko la Iguputo nʼkuwachotsa mʼmanja mwa Farao mfumu ya Iguputo+ ndipo anayamba kulambira* milungu ina.+ 8 Iwo ankatsatira miyambo ya mitundu imene Yehova anaithamangitsa pamaso pa Aisiraeli ndiponso ankatsatira miyambo imene mafumu a Isiraeli anayambitsa.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani