Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb18.03 2
  • March 5-11

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • March 5-11
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18.03 2

March 5-11

Mateyu 20-21

  • Nyimbo Na. 76 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Aliyense Wofuna Kukhala Wamkulu Pakati Panu Ayenera Kukhala Mtumiki Wanu”: (10 min.)

    • Mat. 20:3​—Alembi ndi Afarisi onyada ankasangalala akamalemekezedwa komanso kupatsidwa ulemu “pamsika” (Zithunzi ndi mavidiyo za “pamsika” pa Mat. 20:3, nwtsty)

    • Mat. 20:20, 21​—Atumwi awiri anapempha kuti apatsidwe udindo komanso malo aulemu (Mfundo zimene ndikuphunzira za “mkazi wa Zebedayo,” “mmodzi kudzanja lanu lamanja, wina kumanzere kwanu” pa Mat. 20:20, 21, nwtsty)

    • Mat. 20:25-28​—Yesu anafotokoza kuti otsatira ake ayenera kukhala odzichepetsa (Mfundo zimene ndikuphunzira za “mtumiki” pa Mat. 20:26, nwtsty)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Mat. 21:9​—Kodi anthu amene ankafuula kuti, “M’pulumutseni Mwana wa Davide!” ankatanthauza chiyani? (Mfundo zimene ndikuphunzira za “M’pulumutseni,” “Mwana wa Davide” pa Mat. 21:9, nwtsty)

    • Mat. 21:18, 19​—Kodi n’chifukwa chiyani Yesu anachititsa kuti mtengo wa mkuyu ufote? (jy 244 ¶4-6)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Mat. 20:1-19

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha zimene tinganene.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) lv 36-37 ¶3-4

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 99

  • Zofunika Pampingo: (5 min.)

  • Zimene Gulu Lathu Lachita: (10 min.) Onetsani vidiyo ya Zimene Gulu Lathu Lachita ya March.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 15 ¶1-8

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 53 ndi Pemphero

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani