Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb20.02 4
  • February 10-16

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • February 10-16
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20.02 4

February 10-16

GENESIS 15-17

  • Nyimbo Na. 39 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “N’chifukwa Chiyani Yehova Anasintha Dzina la Abulamu ndi Sarai?”: (10 min.)

    • Gen. 17:1​—Ngakhale kuti Abulamu anali wopanda ungwiro, ankayesetsa kuchita zabwino (it-1 817)

    • Gen. 17:3-5​—Dzina la Abulamu linasinthidwa kukhala Abulahamu (it-1 31 ¶1)

    • Gen. 17:15, 16​—Dzina la Sarai linasinthidwa kukhala Sara (w09 2/1 13)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Gen. 15:13, 14​—Kodi zaka 400 zomwe mbadwa za Abulahamu zinasautsidwa zinayamba liti, nanga zinatha liti? (it-1 460-461)

    • Gen. 15:16​—Kodi “m’badwo wachinayi” wa Abulahamu unabwerera bwanji ku Kanani? (it-1 778 ¶4)

    • Kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Gen. 15:1-21 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi kenako funsani omvera mafunso otsatirawa: Kodi wofalitsayu anagwiritsa ntchito bwanji mafunso? Nanga anagwiritsira ntchito bwanji chitsanzo pophunzitsa?

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo woyamba. Sonyezani mmene mungayankhire munthu amene wanena zinthu zina zomwe anthu amakonda kunena ngati sakufuna kuti tikambirane nawo. (th phunziro 3)

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 5 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo woyamba. Kenako mugawireni kabuku ka Uthenga Wabwino, ndipo sonyezani mmene mungayambitsire phunziro pokambirana naye phunziro 3. (th phunziro 6)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 131

  • “Kodi Mungatani Kuti Banja Lanu Liziyenda Bwino?”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Zimene Mungachite Kuti Mulimbitse Chikondi M’banja Lanu.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lvs mutu 16 ndime 17-22

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 125 ndi Pemphero

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani