Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb20.04
  • April 13-19

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • April 13-19
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20.04

April 13-19

GENESIS 31

  • Nyimbo Na. 112 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Yakobo ndi Labani Anachita Pangano Lamtendere”: (10 min.)

    • Ge 31:44-46​—Yakobo ndi Labani anaunjika mulu wamiyala pomwe anadyerapo chakudya choimira pangano (it-1 883 ¶1)

    • Ge 31:47-50​—Anatchula malowa kuti Galeeda ndiponso Nsanja ya Mlonda (it-2 1172)

    • Ge 31:51-53​—Analonjezana kuti mabanja awo adzakhala mwamtendere

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Ge 31:19​—N’chifukwa chiyani Rakele anaba aterafi a bambo ake? (it-2 1087-1088)

    • Ge 31:41, 42​—Kodi tikuphunzira chiyani kwa Yakobo ngati timagwira ntchito kwa mabwana “ovuta kuwakondweretsa”? (1Pe 2:18; w13 3/15 21 ¶8)

    • Kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Ge 31:1-7 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi kenako funsani omvera mafunso otsatirawa: Kodi mlongoyu anathandiza bwanji munthuyo kuona mmene angagwiritsire ntchito mfundo ya lemba limene anawerenga? Kodi anachita zotani kuti adzapange ulendo wobwereza?

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo woyamba. Sonyezani mmene mungayankhire munthu amene wanena zinthu zina zomwe anthu amakonda kunena ngati sakufuna kuti tikambirane nawo. (th phunziro 4)

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 5 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo woyamba. Kenako mugawireni kabuku ka Uthenga Wabwino n’kuyamba kuphunzira naye phunziro 5. (th phunziro 8)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 77

  • Muzilimbikitsa Amene Afooka : (Osapitirira 20 min.) Nkhani yokambidwa ndi mkulu. Onerani vidiyo yakuti Yehova Amasamalira Nkhosa Zake. Kenako fotokozani mwachikondi mfundo zingapo zapatsamba 14 m’kabuku kakuti Bwererani kwa Yehova.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) ia Mutu 1 ndime 19-27 ndi Mafunso Obwereza

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (Osapitirira 3 min.)

  • Nyimbo Na. 35 ndi Pemphero

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani