Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb20.09 4
  • September 14-20

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • September 14-20
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20.09 4

September 14-20

EKISODO 25-26

  • Nyimbo Na. 18 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Chinthu Chofunika Kwambiri M’chihema”: (10 min.)

    • Eks 25:9​—Yehova anauza Mose mmene ayenera kupangira likasa la pangano (it-1 165)

    • Eks 25:21​—Likasa linali chinthu choyera chosungiramo umboni wopatulika (it-1 166 ¶2)

    • Eks 25:22​—Likasa linkaimira kukhalapo kwa Mulungu (it-1 166 ¶3)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Eks 25:20​—Kodi mmene akerubi analili pachivundikiro cha Likasa n’kutheka kuti zinkasonyeza chiyani? (it-1 432 ¶1)

    • Eks 25:30​—Kodi mkate wachionetsero unali chiyani? (it-2 936)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Eks 25:23-30 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako funsani omvera mafunso otsatirawa: Kodi wofalitsayu wasonyeza bwanji chikondi komanso chifundo? Kodi iye akanachita chiyani kuti asonyeze munthuyu chimodzi mwa Zinthu Zophunzitsira?

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza. (th phunziro 8)

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 5 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza. Kenako gawirani chimodzi mwa Zinthu Zophunzitsira. (th phunziro 11)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 23

  • Zimene Gulu Lathu Lachita: (5 min.) Onerani vidiyo ya Zimene Gulu Lathu Lachita ya September.

  • Zofunika Pampingo: (10 min.)

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (Osapitirira 30 min.) ia 8:22-27 ndi mfundo zobwereza

  • Mawu Omaliza (Osapitirira 3 min.)

  • Nyimbo Na. 128 ndi Pemphero

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani