Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb22.09 2
  • September 5-11

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • September 5-11
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22.09 2

September 5-11

1 MAFUMU 9-10

  • Nyimbo Na. 10 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Tizitamanda Yehova Chifukwa ndi Wanzeru”: (10 min.)

  • Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • 1Mf 10:10, 14​—Kodi pali umboni wotani wosonyeza kuti Baibulo silinakokomeze kuchuluka kwa golide amene Mfumu Solomo anali naye? (w08-CN 11/1 22:4-6)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (4 min.) 1Mf 10:1-13 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Ulendo Woyamba Phunziro la Baibulo​—Sl 37:29. Muziimitsa vidiyoyi nthawi iliyonse imene pali chizindikiro chosonyeza kuti muime n’kufunsa omvera mafunso omwe ali muvidiyoyi.

  • Ulendo Woyamba: (3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha zimene tinganene pa ntchito yapadera yoyambitsa maphunziro a Baibulo. (th phunziro 1)

  • Ulendo Woyamba: (5 min.) Yambani ndi chitsanzo cha zimene tinganene pa ntchito yapadera yoyambitsa maphunziro a Baibulo. Kenako yambitsani phunziro la Baibulo pogwiritsa ntchito phunziro 01 la kabuku kakuti Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale. (th phunziro 13)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 80

  • “Mungapeze Nzeru Zokuthandizani pa JW.ORG”: (8 min.) Nkhani yokambirana. Limbikitsani omvera kuti azifufuza pa jw.org malangizo a m’Baibulo owathandiza kulimbana ndi mavuto amene amakumana nawo.

  • Zofunika Pampingo: (7 min.)

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lff phunziro 09

  • Mawu Omaliza (3 min.)

  • Nyimbo Na. 47 ndi Pemphero

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani