Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • w22.01
  • Magazini Yophunzira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Magazini Yophunzira
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
w22.01
Nsanja ya Olonda Yophunzira, January 2022.

Magazini Yophunzira

JANUARY 2022

NKHANI ZOPHUNZIRA KUYAMBIRA: FEBRUARY 28–APRIL 3, 2022

© 2021 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

LEMBA LA CHAKA CHA 2022:

“Ofunafuna Yehova sadzasowa chilichonse chabwino.”​—SAL. 34:10

Magaziniyi sitigulitsa. Timaipereka ngati njira imodzi yophunzitsira anthu Baibulo padziko lonse ndipo ndalama zoyendetsera ntchitoyi ndi zimene anthu amapereka mwa kufuna kwawo. Ngati mukufuna kupereka pitani pa donate.jw.org.

Malemba onse m’magaziniyi akuchokera mu Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika lolembedwa m’Chichewa chamakono, kupatulapo ngati tasonyeza Baibulo lina.

CHITHUNZI CHAPACHIKUTO:

Pa nthawi ya chisautso chachikulu, Gogi wa ku Magogi adzayesa kutiukira m’nyumba zathu. Koma sitidzachita mantha podziwa kuti Yesu ndi angelo ake akuona zomwe zikuchitika ndipo atiteteza (Onani nkhani yophunzira 1, ndime 13)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani