Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • w23.11 1-32
  • Magazini Yophunzira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Magazini Yophunzira
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
w23.11 1-32
Ezara ndi Aisiraeli ena ali pakachisi, akulira. Sekaniya akuthandiza Ezara kuti aimirire.

Magazini Yophunzira

NOVEMBER 2023

NKHANI ZOPHUNZIRA KUYAMBIRA: JANUARY 8–FEBRUARY 4, 2024

© 2023 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

Magaziniyi sitigulitsa. Timaipereka ngati njira imodzi yophunzitsira anthu Baibulo padziko lonse ndipo ndalama zoyendetsera ntchitoyi ndi zimene anthu amapereka mwa kufuna kwawo. Ngati mukufuna kupereka pitani pa donate.jw.org.

Malemba onse m’magaziniyi akuchokera mu Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika lolembedwa m’Chichewa chamakono, kupatulapo ngati tasonyeza Baibulo lina.

CHITHUNZI CHAPACHIKUTO:

Ezara ali kukachisi ndipo akulira komanso kupemphera chifukwa cha machimo a anthu. Gulu nalonso likulira. Kenako Sekaniya akulimbikitsa Ezara pomuuza kuti: “Aisiraeli ali ndi chiyembekezo . . . ndipo ife tili nawe.”—Ezara 10:​2, 4 (Onani nkhani yophunzira 48, ndime 17)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani