Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • nwt 1705-1706
  • Zimene Zili Mʼbuku la Maliko

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Zili Mʼbuku la Maliko
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Nkhani Yofanana
  • Zimene Zili Mʼbuku la Mateyu
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Zimene Zili Mʼbuku la Luka
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Zimene Zili Mʼbuku la Yohane
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • A7-D Zinthu Zikuluzikulu Zimene Yesu Anachita Ali Padziko Lapansi—Utumiki Waukulu wa Yesu MʼGalileya (Gawo 2)
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Onani Zambiri
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Zimene Zili Mʼbuku la Maliko

MALIKO

ZIMENE ZILI MʼBUKULI

  • 1

    • Yohane Mʼbatizi ankalalikira (1-8)

    • Kubatizidwa kwa Yesu (9-11)

    • Yesu anayesedwa ndi Satana (12, 13)

    • Yesu anayamba kulalikira ku Galileya (14, 15)

    • Anasankha ophunzira oyambirira (16-20)

    • Anatulutsa mzimu wonyansa (21-28)

    • Yesu anachiritsa anthu ambiri ku Kaperenao (29-34)

    • Anapemphera kumalo opanda anthu (35-39)

    • Munthu wakhate anachiritsidwa (40-45)

  • 2

    • Yesu anachiritsa munthu wakufa ziwalo (1-12)

    • Yesu anaitana Levi (13-17)

    • Funso lokhudza kusala kudya (18-22)

    • Yesu ndi ‘Mbuye wa Sabata’ (23-28)

  • 3

    • Munthu wolumala dzanja anachiritsidwa (1-6)

    • Chigulu cha anthu chinali mʼmbali mwa nyanja (7-12)

    • Atumwi 12 (13-19)

    • Kunyoza mzimu woyera (20-30)

    • Mayi komanso azichimwene ake a Yesu (31-35)

  • 4

    • MAFANIZO OKHUDZA UFUMU (1-34)

      • Wofesa mbewu (1-9)

      • Chifukwa chake Yesu ankagwiritsa ntchito mafanizo (10-12)

      • Tanthauzo la fanizo la wofesa mbewu (13-20)

      • Nyale saivindikira ndi dengu (21-23)

      • Muyezo umene mukuyezera (24, 25)

      • Wofesa mbewu amene amagona (26-29)

      • Kanjere ka mpiru (30-32)

      • Anagwiritsa ntchito mafanizo (33, 34)

    • Yesu analetsa mafunde (35-41)

  • 5

    • Yesu anatumiza ziwanda munkhumba (1-20)

    • Mwana wamkazi wa Yairo; mzimayi amene anagwira malaya akunja a Yesu (21-43)

  • 6

    • Yesu anakanidwa mʼdera lakwawo (1-6)

    • Atumwi 12 anapatsidwa malangizo okhudza utumiki (7-13)

    • Imfa ya Yohane Mʼbatizi (14-29)

    • Yesu anadyetsa anthu 5,000 (30-44)

    • Yesu anayenda pamadzi (45-52)

    • Anachiritsa anthu ku Genesareti (53-56)

  • 7

    • Anadzudzula miyambo ya anthu (1-13)

    • Zinthu zimene zimaipitsa munthu zimachokera mumtima (14-23)

    • Chikhulupiriro cha mayi wa Chisurofoinike (24-30)

    • Munthu amene anali ndi vuto losamva anachiritsidwa (31-37)

  • 8

    • Yesu anadyetsa anthu 4,000 (1-9)

    • Anapempha chizindikiro (10-13)

    • Zofufumitsa za Afarisi ndi Herode (14-21)

    • Munthu wavuto losaona anachiritsidwa ku Betsaida (22-26)

    • Petulo anazindikira kuti Yesu ndi Khristu (27-30)

    • Yesu ananeneratu za imfa yake (31-33)

    • Chizindikiro cha wophunzira weniweni (34-38)

  • 9

    • Yesu anasintha maonekedwe ake (1-13)

    • Mnyamata wogwidwa ndi chiwanda anachiritsidwa (14-29)

      • Zinthu zonse ndi zotheka kwa munthu amene ali ndi chikhulupiriro (23)

    • Yesu ananeneratu kachiwiri za imfa yake (30-32)

    • Ophunzira anakangana kuti wamkulu ndi ndani (33-37)

    • Aliyense amene sakulimbana nafe ali kumbali yathu (38-41)

    • Zopunthwitsa (42-48)

    • “Khalani ndi mchere mwa inu nokha” (49, 50)

  • 10

    • Ukwati komanso kutha kwa banja (1-12)

    • Yesu anadalitsa ana (13-16)

    • Funso la munthu wachuma (17-25)

    • Zinthu zimene tikuyenera kudzimana chifukwa cha Ufumu (26-31)

    • Yesu ananeneratunso za imfa yake (32-34)

    • Pempho la Yakobo ndi Yohane (35-45)

      • Yesu anapereka dipo kuti awombole anthu ambiri (45)

    • Batimeyu amene anali ndi vuto losaona anachiritsidwa (46-52)

  • 11

    • Yesu analowa mumzinda mwaulemerero (1-11)

    • Anatemberera mtengo wamkuyu (12-14)

    • Yesu anayeretsa kachisi (15-18)

    • Zimene tikuphunzira pa mtengo wamkuyu umene unafota (19-26)

    • Anatsutsa ulamuliro wa Yesu (27-33)

  • 12

    • Fanizo la alimi amene anapha anthu (1-12)

    • Mulungu komanso Kaisara (13-17)

    • Funso lokhudza kuuka kwa akufa (18-27)

    • Malamulo awiri aakulu kwambiri (28-34)

    • Kodi Khristu ndi mwana wa Davide? (35-37a)

    • Anawachenjeza kuti asamale ndi alembi (37b-40)

    • Timakobidi tiwiri ta mayi wamasiye wosauka (41-44)

  • 13

    • MAPETO A NTHAWI INO (1-37)

      • Nkhondo, zivomerezi, kusowa kwa chakudya (8)

      • Uthenga wabwino ukuyenera kulalikiridwa (10)

      • Chisautso chachikulu (19)

      • Kubwera kwa Mwana wa munthu (26)

      • Fanizo la mtengo wamkuyu (28-31)

      • Khalani maso (32-37)

  • 14

    • Ansembe anakonza zoti aphe Yesu (1, 2)

    • Anathira Yesu mafuta onunkhira kwambiri (3-9)

    • Yudasi anapereka Yesu (10, 11)

    • Pasika womaliza (12-21)

    • Anayambitsa Mwambo wa Chakudya Chamadzulo cha Ambuye (22-26)

    • Ananeneratu zoti Petulo adzamukana (27-31)

    • Yesu anapemphera ku Getsemane (32-42)

    • Yesu anagwidwa (43-52)

    • Anaimbidwa mlandu Mʼkhoti Lalikulu la Ayuda (53-65)

    • Petulo anakana Yesu (66-72)

  • 15

    • Yesu anakaonekera pamaso pa Pilato (1-15)

    • Ananyozedwa pagulu (16-20)

    • Anamukhomerera pamtengo ku Gologota (21-32)

    • Imfa ya Yesu (33-41)

    • Kuikidwa mʼmanda kwa Yesu (42-47)

  • 16

    • Yesu anaukitsidwa (1-8)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani