Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • ll section 11
  • Kodi Yehova Amamvetsera Mapemphero Athu?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Yehova Amamvetsera Mapemphero Athu?
  • Mverani Mulungu Kuti Mudzapeze Moyo Wosatha
  • Nkhani Yofanana
  • Tili Ndi Mwayi Wopemphera kwa Mulungu
    Zimene Baibulo Limaphunzitsa
  • Pemphero Lingakuthandizeni Kuti Mulungu Akhale Mnzanu
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
  • Kodi Mungatani Kuti Mulungu Azimvetsera Mapemphero Anu?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2021
  • Muziyamikira Mwayi Wanu wa Pemphero
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
Mverani Mulungu Kuti Mudzapeze Moyo Wosatha
ll section 11

CHIGAWO 11

Kodi Yehova Amamvetsera Mapemphero Athu?

Mulungu amamva mapemphero athu. 1 Petulo 3:12

Mpando wachifumu  wa Yehova

Yehova ndi “Wakumva pemphero.” (Salimo 65:2) Iye amafuna kuti tizimuuza zakukhosi kwathu.

Munthu akupemphera

Muzipemphera kwa Yehova yekha osati kwa wina aliyense.

  • Yesu anatiphunzitsa mmene tingapempherere.—Mateyu 6:9-15.

  • Kodi Mulungu amamvetsera mapemphero a ndani?​—Salimo 145:18, 19.

Pali zinthu zambiri zimene tingatchule popemphera. 1 Yohane 5:14

Yesu ndi a 144,000 mu Ufumu wake

Muzipemphera kuti chifuniro cha Mulungu chichitike kumwamba komanso padziko lapansi pano.

Muzipemphera m’dzina la Yesu, kuti musonyeze kuti mumayamikira zimene iye anakuchitirani.

Mkhristu amene amadalira Yehova kuti amuthandize komanso amathandiza banja lake ndipo amachita zabwino

Pemphani Yehova kuti akuthandizeni kuchita zinthu zabwino. Mungapemphe zinthu monga chakudya, ntchito, nyumba, zovala ndiponso thanzi labwino.

  • Yehova amamva mapemphero a anthu amene amachita zolungama.​—Miyambo 15:29.

  • Musamade nkhawa.​—Afilipi 4:6, 7.

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani