Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • lfb sect. 8
  • Mawu Oyamba Gawo 8

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Oyamba Gawo 8
  • Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Nkhani Yofanana
  • Solomo Anali Mfumu Yanzeru
    Kodi Baibulo Lili Ndi Uthenga Wotani?
  • Nyumba ya Yehova
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Zimene Zili Mʼbuku la 1 Mafumu
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Analimbikitsidwa ndi Mulungu Wake
    Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo
Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
lfb sect. 8
Mfumu Solomo inapeza mayi weniweni wa mwana

Mawu Oyamba Gawo 8

Yehova anadalitsa Solomo pomupatsa nzeru komanso mwayi woti adzamange kachisi. Koma patapita nthawi Solomo anasiya kulambira Yehova. Ngati ndinu kholo, fotokozerani mwana wanu mmene anthu olambira milungu yabodza anachititsira kuti Solomo asiye kulambira Yehova. Ufumu wa Isiraeli unagawanika ndipo mafumu oipa anachititsa kuti anthu asiye kulambira Mulungu n’kumalambira mafano. Pa nthawi imeneyo, atumiki ambiri a Yehova ankazunzidwa kapenanso kuphedwa kumene. Mfumukazi Yezebeli inachititsa kuti anthu a mu ufumu wakumpoto azilambira kwambiri mafano. Imeneyi inali nthawi yovuta kwambiri kwa Aisiraeli. Komabe panali anthu ena amene ankatumikira Yehova mokhulupirika. Ena mwa anthuwa anali Mfumu Yehosafati komanso mneneri Eliya.

ZIMENE TIPHUNZIRE M’CHIGAWOCHI

  • Muzitumikira Yehova mokhulupirika ngakhale anthu a m’banja lanu kapena anzanu atasiya kumutumikira

  • Mukasiya kutumikira Yehova, palibe chimene chingayende. Koma mukamamutumikirabe adzakudalitsani

  • Nthawi zambiri munthu akamaona kuti akusowa mtengo wogwira, Yehova amamuthandiza m’njira yoti samayembekezera

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani