Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • sjj 117
  • Khalidwe la Ubwino

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khalidwe la Ubwino
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Tingatani Kuti ‘Tilawe’ Ubwino wa Yehova?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj 117

NYIMBO 117

Khalidwe la Ubwino

zosindikizidwa

(2 Mbiri 6:41)

  1. 1. Yehova M’lungu wabwino

    Mumatidalitsadi.

    Ndinu wokhulupirika,

    Mumachita zabwino.

    Mumasonyeza chifundo

    Kwa anthu ochimwafe.

    Tilambire inu nokha.

    Tikutumikireni.

  2. 2. Taona ubwino wanu

    Mwa atumiki anu.

    Khalidwe lawo labwino

    Limatilimbikitsa.

    Mwatipatsa Mawu anu

    Ndi abusa abwino.

    Mutipatse mzimu wanu

    Tizichita zabwino.

  3. 3. Chonde muzitidalitsa

    Tikachita zabwino.

    Tikhale okoma mtima

    Kwa munthu aliyense.

    M’mabanja ndi mumipingo

    Ndiponso kulikonse,

    Muzitithandiza kuti

    Tizichita zabwino.

(Onaninso Sal. 103:10; Maliko 10:18; Agal. 5:​22; Aef. 5:9.)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani