Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • sjj 160
  • “Uthenga Wabwino”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Uthenga Wabwino”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Ndi Ndani Amene Amalalikira Uthenga Wabwino?
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj 160

NYIMBO 160

“Uthenga Wabwino”

zosindikizidwa

(Luka 2:10)

  1. 1. Tilemekeze M’lungu

    Amatikonda.

    Anatumiza Mwana wake

    Kudzatipatsa

    Chiyembekezochi.

    (KOLASI)

    Uthengawu ndi

    Wosangalatsa.

    Ndi wabwinodi.

    Tilalikire

    Za uthengawu.

    Khristu wabadwa,

    Mpulumutsi wathu.

  2. 2. Azidzalamulira

    Mwachilungamo.

    Abweretsa Paradaiso

    Ndipo Ufumu

    Wakewo sudzatha.

    (KOLASI

    Uthengawu ndi

    Wosangalatsa.

    Ndi wabwinodi.

    Tilalikire

    Za uthengawu.

    Khristu wabadwa,

    Mpulumutsi wathu.

    (KOLASI)

    Uthengawu ndi

    Wosangalatsa.

    Ndi wabwinodi.

    Tilalikire

    Za uthengawu.

    Khristu wabadwa,

    Mpulumutsi wathu.

(Onaninso Mat. 24:14; Yoh. 8:12; 14:6; Yes. 32:1; 61:2.)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani