Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb18.07 1
  • Zimene Tinganene

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Tinganene
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • ●○○ ULENDO WOYAMBA
  • ○●○ ULENDO WOBWEREZA WOYAMBA
  • ○○● ULENDO WOBWEREZA WACHIWIRI
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18.07 1
Mabanja a Mboni za Yehova ochokera m’mayiko osiyanasiyana ali ku Msonkhano Wapadera ku Vienna m’dziko la Austria

Msonkhano wapadera mumzinda wa Vienna ku Austria

Zimene Tinganene

●○○ ULENDO WOYAMBA

Funso: Kodi anthu okwatirana angatani kuti banja lawo likhale lolimba?

Lemba: Aef. 5:33

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi makolo angatani kuti ana awo akule bwino?

○●○ ULENDO WOBWEREZA WOYAMBA

Funso: Kodi makolo angatani kuti ana awo akule bwino?

Lemba: Miy. 22:6

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi ana angatani kuti zinthu ziziwayendera bwino?

○○● ULENDO WOBWEREZA WACHIWIRI

Funso: Kodi ana angatani kuti zinthu ziziwayendera bwino?

Lemba: Miy. 4:5, 6

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi ndi kuti kumene tingapeze malangizo amene angatithandize pa moyo wathu?

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani