Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb21.01 23
  • Kodi Mungatsanzire Bwanji Anaziri?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mungatsanzire Bwanji Anaziri?
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Nkhani Yofanana
  • Zimene Tingaphunzire kwa Anaziri
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
  • Yehova Amasintha Temberero N’kukhala Dalitso
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Utumiki wa Alevi
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Zimene Tingaphunzire pa Zomwe Zinkachitika pa Msasa wa Aisiraeli
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21.01 23

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Kodi Mungatsanzire Bwanji Anaziri?

Anaziri ankalolera kudzimana zinthu zina (Nu 6:​2-4; it-2 477)

Anaziri ankagonjera n’kumatsatira zofuna za Yehova (Nu 6:5)

Anaziri ankachita zonse zimene Yehova ankafuna kuti akhalebe oyera (Nu 6:​6, 7)

Masiku ano, Akhristu amene ali muutumiki wa nthawi zonse amasonyeza mtima wodzimana ndipo amagonjera Yehova komanso dongosolo lake.

Abale ndi alongo a mu utumiki wa nthawi zonse. 1. Apainiya awiri akulalikira bambo amene ali pabulu. 2. M’bale ndi mlongo akugwira ntchito ya zomangamanga.
    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani