Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb22.07 18
  • Nzeru Ndi Zamtengo Wapatali

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nzeru Ndi Zamtengo Wapatali
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • Solomo Anapemphera Modzichepetsa Komanso Mochokera Pansi pa Mtima
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Anagwira Ntchito Mwamphamvu Komanso ndi Mtima Wonse
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Solomo Anali Mfumu Yanzeru
    Kodi Baibulo Lili Ndi Uthenga Wotani?
  • B8 Kachisi Amene Solomo Anamanga
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22.07 18
Mfumu Solomo ikuweruza mlandu wa mahule awiri amene onse akunena kuti mwana ndi wawo.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Nzeru Ndi Zamtengo Wapatali

Solomo anapempha nzeru kwa Yehova (1Mf 3:7-9; w11 12/15 8 ¶4-6)

Yehova anasangalala ndi zimene Solomo anapempha (1Mf 3:10-13)

Aisiraeli ankakhala mwabata chifukwa chakuti Solomo ankagwiritsa ntchito nzeru zimene Mulungu anamupatsa (1Mf 4:25)

Kukhala wanzeru kumatanthauza kudziwa zinthu ndi kuzimvetsa bwinobwino kenako n’kuzigwiritsa ntchito moyenera. Nzeru ndi zamtengo wapatali kuposa golide. (Miy 16:16) Kuti tipeze nzeru tiyenera kumupempha Mulungu, kumamuopa, kukhala odzichepetsa komanso kuphunzira mozama Mawu ake.

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani