Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb23.03 17
  • Muzitsatira Malangizo Anzeru

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzitsatira Malangizo Anzeru
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • ‘Mtima Wanga Udzakhala Pamenepa Nthawi Zonse’
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Mfumu Solomo Inasankha Zinthu Mopanda Nzeru
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Ufumu Unagawikana
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • “Khulupirirani Yehova Mulungu Wanu”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23.03 17

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Muzitsatira Malangizo Anzeru

Rehobowamu anafunika kusankha zochita (2Mb 10:1-4; w18-CN.06 13:3)

Rehobowamu anafunsira malangizo (2Mb 10:6-11; w01-CN 9/1 28-29)

Rehobowamu ndi anthu ena anakumana ndi mavuto chifukwa iye sanatsatire malangizo anzeru (2Mb 10:12-16; it-2 768:1)

Mlongo wachitsikana akumvetsera mwachidwi pamene mlongo wachikulire akulankhula ku malo odyera.

Chifukwa cha luso komanso msinkhu wawo, Akhristu olimba mwauzimu nthawi zina akhoza kudziwiratu mmene zinthu zingathere.​—Yob 12:12.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndi ndani mumpingo amene angandipatse malangizo abwino?’

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani