Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb23.09 16
  • Samalani ndi Nkhani Zabodza

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Samalani ndi Nkhani Zabodza
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Musamatsanzire Elifazi Potonthoza Ena
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • ‘Kodi Munthu Angakhale Waphindu kwa Mulungu?’
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • ‘Mukathamangitse Anthu Onse a M’dzikolo’
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Zimene Yobu Anachita Kuti Akhalebe Woyera
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23.09 16

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Samalani ndi Nkhani Zabodza

Zimene Elifazi ankanena zinkaoneka ngati zoona chifukwa anali wamkulu komanso wanzeru (Yob 4:1; it-1 713:11)

Ziwanda zinamutsogolera kuti akapereke uthenga wofooketsa kwa Yobu (Yob 4:​14-16; w05-CN 9/15 26:2)

Zina mwa zomwe Elifazi ananena zinali zoona, koma anazigwiritsa ntchito molakwika (Yob 4:19; w10-CN 2/15 19:5-6)

M’bale akuyang’ana pafoni yake.

Dziko la Satanali limafalitsa nkhani zabodza zowononga.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndimapeza nthawi yoti nditsimikizire kaye ngati nkhani zimene ndikumva kapena kuwerenga zilidi zoona?’—mrt 32 ¶13-17

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani