Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb23.11 12
  • Kodi Muli ndi Mbiri Ngati ya Yobu?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Muli ndi Mbiri Ngati ya Yobu?
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • “Yembekezera Yehova”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • Kodi Yobu Anali Ndani?
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23.11 12
Yobu akupereka chakudya kwa mzimayi wosauka ndi mwana wake pageti la mumzinda.

Yobu akusonyeza anthu ovutika chikondi chokhulupirika

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Kodi Muli ndi Mbiri Ngati ya Yobu?

Yobu ankapatsidwa ulemu ndi anthu ena (Yob 29:​7-11)

Yobu ankadziwika kuti ankasonyeza anthu ovutika chikondi chokhulupirika (Yob 29:​12, 13; w02 5/15 22 ¶19; onani chithunzi chapachikuto)

Yobu ankachita zinthu mwachilungamo (Yob 29:14; it-1 655 ¶10)

Zithunzi zosonyeza mlongo wachitsikana akuthandiza ena: 1. Akuthandiza mlongo wachikulire pamene akuyendera limodzi. 2. Akumvetsera pamene mlongo wina akufotokoza nkhawa zake. 3. Ali limodzi ndi mlongo wina ndipo akulalikira mzimayi amene akuyenda ndi galu wake. 4. Akupereka chakudya kwa alendo amene abwera kunyumba kwawo.

Kukhala ndi mbiri yabwino n’kofunika kwambiri. (w09 2/1 15 ¶3-4) Timakhala ndi mbiri yabwino ngati kwanthawi yaitali tasonyeza kuti timachita zinthu zoyenera

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndi makhalidwe ati amene ndimadziwika nawo?’

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani