Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Polemba buku lake la Uthenga Wabwino, Luka anatchula Teofilo kuti ndi “wolemekezeka kwambiri.” (Luka 1:3) Anthu ena amaganiza kuti mwina Teofilo anali ndi udindo winawake, ndipo pa nthawiyo anali asanakhale wokhulupirira. Koma polemba buku la Machitidwe, Luka anangomutchula kuti “a Teofilo.” Akatswiri ena a Baibulo amaganiza kuti Teofilo anakhala wokhulupirira atawerenga Uthenga Wabwino wa Luka. Iwo amati n’chifukwa chake Luka sanam’tchulenso ndi mawu aulemu akuti “wolemekezeka kwambiri,” koma anamulembera monga m’bale wake wauzimu.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani