Mawu a M'munsi
c Sitinganene kuti munthu wa ku Itiyopiyayu anapupuluma kubatizidwa, chifukwa anali atalowa kale Chiyuda, ndipo ankadziwa ulosi wonena za Mesiya komanso Malemba ena ambiri. Choncho atadziwa udindo wa Yesu pokwaniritsa chifuniro cha Mulungu, iye anabatizidwa nthawi yomweyo.