Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

c Bwalo la Areopagi linali kumpoto chakumadzulo kwa malo otchedwa Akuropolisi ndipo n’kumene akuluakulu a mzinda wa Atene ankakumana. Mawu akuti “Areopagi” angatanthauze khotilo kapena phiri limene panali bwalolo. Akatswiri amanena zosiyanasiyana zokhudza kumene Paulo anam’tengera. Ena amati anapita naye kuphiri limeneli kapena kumalo ena pafupi ndi phirili, pamene ena amati anapita naye kumalo ena kumene khotili linkakumana, mwina kumsika.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani