Mawu a M'munsi
d Luka ananena kuti mabukuwo anali a ndalama zasiliva zokwana 50,000. Ngati ndalama zake zinali madinari, ndiye kuti munthu ankafunika kugwira ntchito tsiku lililonse kwa masiku 50,000, zomwe ndi zaka pafupifupi 137, kuti apeze ndalama zimenezo.