Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Anthu ambiri sazindikira kuti mawu opezeka pa Yohane 7:53 ndi 8:1-11 sapezeka m’mipukutu yoyambirira ya Baibulo koma anthu anachita kuwonjezera. Anthu ena akawerenga nkhaniyi amaganiza kuti munthu amene sanachimwepo ndi amene ayenera kuweruza munthu amene wachita chigololo. Koma lamulo limene Yehova anapereka kwa Aisiraeli linali lakuti: “Mwamuna akapezeka akugona ndi mkazi wa mwiniwake, mwamuna ndi mkaziyo, onsewo azifera pamodzi.”​—Deut. 22:22.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani