Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

b N’zodziwikiratu kuti anthu ena amene adzapulumuke nkhondo ya Aramagedo adzakhala olumala. Yesu ali padzikoli, anachiritsa anthu okhala ndi “zofooka zilizonse” ndipo zimenezi zikusonyeza zimene iye adzachitire anthu opulumuka pa Aramagedo, osati oukitsidwa. (Mat. 9:35) N’zosakayikitsa kuti anthu amene anamwalira adzaukitsidwa ndi matupi abwinobwino.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani