Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Anthu ofufuza zinthu zakale anapeza zokolola zambiri zimene zinakwiririka pamalo amene panali mzinda wa Yeriko ndipo izi zikusonyeza kuti mzindawu sunazunguliridwe ndi Aisiraeli kwa nthawi yaitali moti chakudya sichinathe mumzindawo. Popeza Aisiraeli sanaloledwe kulanda zinthu mumzinda wa Yeriko, nthawi imene anagonjetsa mzindawu inali yabwino chifukwa m’minda munali chakudya chambirimbiri.​—Yos. 5:10-12.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani