Mawu a M'munsi
c TANTHAUZO LA MAWU ENA: Malonjezo a Yehova ndi mawu amene iye amanena osonyeza kuti zinthu zinazake zidzachitikadi. Malonjezo amenewa angatithandize kuti tisamade nkhawa ndi mavuto amene tingakumane nawo pa moyo wathu.
c TANTHAUZO LA MAWU ENA: Malonjezo a Yehova ndi mawu amene iye amanena osonyeza kuti zinthu zinazake zidzachitikadi. Malonjezo amenewa angatithandize kuti tisamade nkhawa ndi mavuto amene tingakumane nawo pa moyo wathu.