Mawu a M'munsi
d MAWU A M’MUNSI: Mawu oti “Usachite mantha” amapezeka katatu pa Yesaya 41:10, 13 ndi 14. Mavesi amenewa amanenanso kuti “Ine” mobwerezabwereza (kutanthauza Yehova). N’chifukwa chiyani Yehova anachititsa kuti Yesaya anene mawu akuti “Ine” mobwerezabwereza? Anachita zimenezi pofuna kutsindika kuti tiyenera kudalira Yehova kuti tisamachite mantha.