Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

d MAWU A M’MUNSI: Mawu oti “Usachite mantha” amapezeka katatu pa Yesaya 41:10, 13 ndi 14. Mavesi amenewa amanenanso kuti “Ine” mobwerezabwereza (kutanthauza Yehova). N’chifukwa chiyani Yehova anachititsa kuti Yesaya anene mawu akuti “Ine” mobwerezabwereza? Anachita zimenezi pofuna kutsindika kuti tiyenera kudalira Yehova kuti tisamachite mantha.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani