Mawu a M'munsi
a Iyi ndi nkhani yoyamba pa nkhani 4 zimene tikambirane zosonyeza kuti Yehova amatikonda kwambiri. Nkhani zina zidzatuluka mu Nsanja ya Olonda ya May 2019. Mitu ya nkhanizo ndi yakuti “Tizisonyeza Chikondi ndi Chilungamo Mumpingo Wachikhristu,” “Tizisonyeza Chikondi ndi Chilungamo M’dziko Loipali” ndiponso “Tizilimbikitsa Anthu Amene Achitiridwa Zoipa.”