Mawu a M'munsi
c CHITHUNZI PATSAMBA LOYAMBA: Yehova ankafuna kuti makolo azikonda ana awo komanso kuwaphunzitsa n’cholinga choti anawo azikhala otetezeka
MAWU OFOTOKOZERA CHITHUNZI: Mayi wachiisiraeli akucheza ndi ana ake uku akukonza chakudya. Chakumbuyo kwawo, bambo akuphunzitsa mwana wake kusamalira nkhosa.