Mawu a M'munsi
a Kusankha kuti mubatizidwe kapena ayi ndi nkhani yaikulu kwambiri kuposa nkhani ina iliyonse. Munkhaniyi tikambirana chifukwa chake tikunena zimenezi. Ithandizanso anthu amene akufuna kubatizidwa kuthana ndi mavuto amene angawalepheretse kuchita zimenezi.