Mawu a M'munsi
a Satana ndi ziwanda zake akhala akunamiza anthu pa nkhani ya zimene zimachitika munthu akamwalira. Mabodza amenewa achititsa kuti anthu azichita miyambo yosemphana ndi Malemba. Nkhaniyi itithandiza kuti tizikhalabe okhulupirika kwa Yehova pamene anthu akutikakamiza kuti tichite nawo miyamboyi.