Mawu a M'munsi
b Nawonso abale ambiri achikulire asiyira udindo wawo abale achinyamata. Onani nkhani yakuti “Akhristu Achikulire, Yehova Amayamikira Kukhulupirika Kwanu,” mu Nsanja ya Olonda ya September 2018 ndiponso yakuti “Tizikhalabe ndi Mtendere Wamumtima Zinthu Zikasintha,” mu Nsanja ya Olonda ya October 2018.