Mawu a M'munsi
d Kuti mudziwe bwinobwino zimene zidzachitike nkhondo ya Aramagedo isanayambe, onani mutu 21 m’buku lakuti Ufumu wa Mulungu Ukulamulira. Kuti mudziwe zambiri zokhudza kuukira kwa Gogi wakudziko la Magogi komanso mmene Yehova adzatetezere anthu ake pa Aramagedo, onani Nsanja ya Olonda ya July 15, 2015, tsamba 14-19.