Mawu a M'munsi
a DZIWANI IZI: Ngakhale kuti mukhoza kusankha kugwiritsa ntchito kachigawo kakuti “Onani Zinanso” pa nthawi ya phunziro, muziyesetsa kupeza nthawi yowerenga komanso kuonera mavidiyo onse pamene mukukonzekera. Kuchita zimenezi kungakuthandizeni kudziwa zimene zingafike pamtima komanso kuthandiza wophunzira wanuyo. M’kabuku komanso m’buku la pazipangizo zamakono muli malinki a mavidiyo komanso zinthu zina zowonjezera.