Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

c MAWU OFOTOKOZERA CHITHUNZI: Onani mmene kuphunzira Baibulo kungathandizire munthu kusintha moyo wake: Poyamba munthuyu akuona kuti moyo wake ulibe cholinga chifukwa sadziwa Yehova. Kenako wakumana ndi a Mboni omwe akulalikira ndipo wavomera kuti aziphunzira Baibulo. Zimene waphunzira zamuthandiza kuti adzipereke kwa Yehova ndipo akubatizidwa. M’kupita kwa nthawi nayenso akuthandiza ena kuti akhale ophunzira a Yesu. Pamapeto pake onse akusangalala m’Paradaiso.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani