Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Kodi munayamba mwamvapo Mkhristu amene watumikira Yehova kwa nthawi yayitali akunena kuti, ‘Sindinkayembekezera kuti dziko loipali likhala lilipobe mpaka pano.’ Tonsefe timafunitsitsa Yehova atawononga dziko loipali makamaka munthawi yovutayi. Komabe tiyenera kuphunzira kukhala oleza mtima. Munkhaniyi tikambirana mfundo za m’Baibulo zimene zingatithandize kuyembekezera nthawi imene Yehova adzachitepo kanthu. Tikambirananso mbali ziwiri zimene tiyenera kuyembekezera Yehova moleza mtima komanso madalitso amene anthu omwe amamuyembekezera adzapeze.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani