Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Yehova ndi mnzathu wapamtima. Timaona kuti ubwenzi wathu ndi iye ndi wamtengo wapatali ndipo timafunitsitsa kuti timudziwe bwino. Pamatenga nthawi yaitali kuti tidziwane bwino ndi winawake. Choncho pangafunike nthawi yokwanira kuti tipitirize kulimbitsa ubwenzi wathu ndi Yehova. Popeza kuti masiku ano timakhala otanganidwa kwambiri, kodi tingatani kuti tizipeza nthawi yolimbitsa ubwenzi wathu ndi Atate wathu wakumwamba? Nanga kuchita zimenezi kungatithandize bwanji?

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani