Mawu a M'munsi
a Tonsefe tingapindule poona zimene ena akuchita potumikira Yehova. Koma tiyenera kupewa kudziyerekezera ndi ena. Nkhaniyi itithandiza kuti tizisangalalabe n’kumapewa mtima wonyada kapena kufooka chifukwa choyerekezera zimene ena akuchita ndi zimene ife tikuchita.