Mawu a M'munsi
a Iyi ndi nkhani yomaliza pa nkhani zitatu zomwe zikufotokoza buku la Chivumbulutso. Monga mmene tionere munkhaniyi, anthu omwe apitirize kukhalabe okhulupirika kwa Yehova adzakhala ndi tsogolo labwino, koma amene amatsutsa ulamuliro wa Mulungu adzawonongedwa mochititsa manyazi.