Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Tikamaganizira za munthu yemwe anapirira mayesero aakulu, nthawi zambiri timaganizira za Yobu. Kodi timaphunzira chiyani pa zimene zinamuchitikira? Timaphunzira kuti Satana sangatikakamize kusiya kutumikira Yehova, komanso kuti Yehovayo amadziwa chilichonse chomwe chikutichitikira. Ndipo mofanana ndi mmene anathetsera mavuto a Yobu, tsiku lina adzathetsanso mavuto athu onse. Zochita zathu zikamasonyeza kuti timakhulupirira kwambiri mfundozi, timakhala m’gulu la anthu omwe ‘amayembekezera Yehova.’

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani